Banja La Chitsanzo Banja La Chitsanzo

Banja La Chitsanzo

    • $16.500
    • $16.500

Descripción editorial

Mu bukhu lapamwambali, Dag Heward-Mills akupereka kuzindikira kwakukulu kwa zochitika m'banja. Bukhu lodabwitsali likagwira ntchito ngati chipangizo chokonzekera kwa phungu wa banja ndi anthu okwatira. Inu mukapeza mu bukhuli, mfundo zotsitsimutsa ndi zosangalatsa zopititsa patsogolo banja lanu.

"Bukhu ili ndilodzadza ndi nkhani pa maziko ndi zochitika pa maubwenzi a umunthu mu nthawi imene musanakwatire, muli m'banja ndi ngakhale utatha ukwati. Ili ndi zipangizo zofufuzidwa bwino ndi zovomerezeka pa thunthu ndi kakhalidwe kazolengedwa pazogonana, kubereka kwa anthu, mimba ndi nthawi yobereka ikadutsa. Kuthekera kwa Dotolo Dag Heward-Mills kusintha nkhani zovuta kukhala zophweka ndiye chikhalidwe chosiyanitsa pa bukhuli. Zonse pamodzi, izi zimalipangitsa kukhala bukhu losindikizika lomveka kwambiri, logwiritsika ntchito bwino pa zabanja lero." David Asomani, katswiri wowona za chiberekero cha azimayi.

"Bukhu la Bishopu Dag Heward-Mills pa uphungu wa m'banja ndilosowa chifanizo. Maziko ake ngati dotolo wa zachipatala zawonetsedwa momveka bwino mu tsatanetsatane, koma kudzifotokozera kwa zizindikiro zachipatala zomwe zikupangitsa bukhuli kukhala lapadera." Edwin Morgan Ogoe, Mphunzitsi, Sukulu Yaukachenjede ya Ghana, Sukulu Yazachipatala

GÉNERO
Religión y espiritualidad
PUBLICADO
2020
4 de febrero
IDIOMA
NY
Nyanja
EXTENSIÓN
241
Páginas
EDITORIAL
Dag Heward-Mills
VENDEDOR
Draft2Digital, LLC
TAMAÑO
3.6
MB

Más libros de Dag Heward-Mills

Lealtad y Deslealtad Lealtad y Deslealtad
2016
Por qué los cristianos que no diezman empobrecen…y cómo prosperan los cristianos que diezman Por qué los cristianos que no diezman empobrecen…y cómo prosperan los cristianos que diezman
2016
Hija, tú puedes lograrlo Hija, tú puedes lograrlo
2016
Los que se ofenden Los que se ofenden
2023
El Arte de Pastorear El Arte de Pastorear
2016
Atrapa La Unción Atrapa La Unción
2011