Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa

Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa

    • USD 8.99
    • USD 8.99

Descripción editorial

Chinthu chimodzi chokha chimadza kwa inu mukamva mawu akuti "M’busa" - nkhosa! Nkhosa ndi nyama zodalira zome zimafunikira abusa. M’busa ndi wotsogolera wosamalira komanso wachikondi kwa nkhosa. M'Baibulo, Mulungu amatitchula ife ngati gulu la nkhosa za Mulungu.
Yesu adamuuza wophunzira Petro kuti adyetse nkhosa zake kuti atsimikizire za chikondi chake cha Mpulumutsi. Kukhala m'busa ndi ntchito yabwino kwambiri. Ndi chinthu chapamwamba kuitanidwa ndi Mulungu ndi kulembetsedwa mwa antchito Ake ndi kusamalira nkhosa.
Mu bukhuli, Dag Heward-Mills akutiitanira ife, akutilimbikitsa ndi kutiwonetsa ife momwe tingatengerepo nawo mbali pa ntchito yayikulu yosamalira anthu a Mulungu. Musati muzisiyidwe kunja kwa ntchito yabwino iyi yokhala m’busa!

GÉNERO
Religión y espiritualidad
PUBLICADO
2019
21 de noviembre
IDIOMA
NY
Nyanja
EXTENSIÓN
125
Páginas
EDITORIAL
Dag Heward-Mills
VENDEDOR
Draft2Digital, LLC
TAMAÑO
472.1
KB

Más libros de Dag Heward-Mills

Atrapa La Unción Atrapa La Unción
2011
La unción y la presencia La unción y la presencia
2022
Los que te honran (Lealtad y Deslealtad) Los que te honran (Lealtad y Deslealtad)
2022
Conoce a tus enemigos invisibles... ¡y derrótalos! Conoce a tus enemigos invisibles... ¡y derrótalos!
2018
Cómo tener un efectivo tiempo devocional diario con Dios Cómo tener un efectivo tiempo devocional diario con Dios
2018
Ética Ministerial Ética Ministerial
2018