Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa

Zomwe Zikutanthauza Kukhala M’busa

    • €7.49
    • €7.49

Publisher Description

Chinthu chimodzi chokha chimadza kwa inu mukamva mawu akuti "M’busa" - nkhosa! Nkhosa ndi nyama zodalira zome zimafunikira abusa. M’busa ndi wotsogolera wosamalira komanso wachikondi kwa nkhosa. M'Baibulo, Mulungu amatitchula ife ngati gulu la nkhosa za Mulungu.
Yesu adamuuza wophunzira Petro kuti adyetse nkhosa zake kuti atsimikizire za chikondi chake cha Mpulumutsi. Kukhala m'busa ndi ntchito yabwino kwambiri. Ndi chinthu chapamwamba kuitanidwa ndi Mulungu ndi kulembetsedwa mwa antchito Ake ndi kusamalira nkhosa.
Mu bukhuli, Dag Heward-Mills akutiitanira ife, akutilimbikitsa ndi kutiwonetsa ife momwe tingatengerepo nawo mbali pa ntchito yayikulu yosamalira anthu a Mulungu. Musati muzisiyidwe kunja kwa ntchito yabwino iyi yokhala m’busa!

GENRE
Religion & Spirituality
RELEASED
2019
21 November
LANGUAGE
NY
Nyanja
LENGTH
125
Pages
PUBLISHER
Dag Heward-Mills
SIZE
472.1
KB

More Books by Dag Heward-Mills

Steps to the Anointing Steps to the Anointing
2011
The Anointing and the Presence The Anointing and the Presence
2019
Labour to be Blessed: Labour not to be rich Labour to be Blessed: Labour not to be rich
2019
Church Growth Church Growth
2011
Read Your Bible, Pray Every Day Read Your Bible, Pray Every Day
2018
A Arte ​de Ouvir (Segunda Edição) A Arte ​de Ouvir (Segunda Edição)
2016